Zabwino ndi Zoipa Chosseketsa Buku

Nsembe. Nkhondo. Mayesero. Chiwembu. Chiyembekezo. Chipulumutso.

Mulungu anasankha kudzivumbulutsa yekha kwa anthu, osati kudzera mu mfundo zokhazikika chabe, kapena m’nzeru chabe, kapenanso m’ziphunzitso chabe, koma makamaka kudzera m’nkhani za uneneri, nkhondo, chifundo, chiweruzo, zozizwitsa, imfa, moyo, ndi chikhululukiro. Nkhani ya mmene Mulungu anakonzera kupulumutsa anthu yafotokozedwa mwatsatanetsatane kuchokera m’buku la Genesis mpaka Chivumbulutso.

Buku limeneli limakuthandizani kudziwa mwatsatenetsatane nkhani yonse ya m’Baibulo mosavuta. Limaonetsa nkhani zikukuzikulu m’njira yosavuta kutsatira yonga ngati sewero.

Werengani tsopano!
English Good and Evil

MUTU 1

CHIYAMBI

English Good and Evil

MUTU 2

ABRAHAMU NDI ISAKI

Chapter 3

MUTU 3

MOSE

Chapter 4 G&E Comic book

MUTU 4

EKSODO

Chapter 5

MUTU 5

UFUMU

Good and Evil Chapter 6

MUTU 6

ELIYA

Good and Evil Chapter 7

MUTU 7

UNENERI WOKHUDZA KHRISTU

Good and evil Chapter 8

MUTU 8

CHIPANGANO CHATSOPANO

Chapter 9 of good and evil

MUTU 9

UTUMIKI WOYAMBIRIRA

Good and evil comic bible

MUTU 10

ZOZIZWITSA NDI MAFANIZO

Good and Evil comic book

MUTU 11

PASKHA NDI MASAUTSO KHRISTU

Chapter 12 Illustrated Bible storybook

MUTU 12

KUUKA KWA AKUFA NDI MPINGO WOYAMBIRIRA

Chapter 13 Illustrated Bible storybook

MUTU 13

KU DZIKO LONSE LAPANSI

Onerani kanema waulere pa intaneti wonena za Yesu.